Back to search (Gauteng > Johannesburg > Charity Donations> ad 1273611606)
To match water
Reason for Reporting
Ufulu ake sitikwawona anthu anu akamadanda ula kuti tilibe chakudja inu mumati musapepuse malawi kuli chakudja kuno . Chosecho achimwene anu m'mimba muku bwata mukha ndi njala ,chemwali ,akholo,agogo,dzidzukhuru ndi adzizanu wose mumati inu azelu . Koma bwanji iwe wekha kumaziwona ngati wazelu.Chosecho mumachita kuthandizida kuti muwoneke mmene muwonekeramo. Muziyamikha chomwe amakupangira mulungu mulungu sangandisiye ndekha mulungu ali nane. Ollo anthu oyipaa!!!! Inu opanda chisoni ndi chifundo pomarangula dza ine ndi nayamba ndatenga china chake kwanukho kuti uku gulu ranga likufuna dzopusa zakodzo ufune wina amene muzimu panga kuti aziva zakhodzo zopusanzo. Mukama wona enawo siuhule ayi ngani ndi mapudzilo . Gulupu iyi IMAPANGA CHINDUCHIMODZI KWA DZONSE (1) KUVA UTHENGE WAMALILO.....(2)KUKHA MBIRANA NGANI ZAZIKO...............................................(3)KHUULULA SIMENE AMATI ZACHISISI.........................................(4)KUFOTOKOZA NDONDO MEKHO NDI M'MENE ZINAKHALIR Mukhana khala inu mukhana tani kuwona banja la anu likhupedwa popanda cholakwa?Zinabwela zigawe zina 4 Zita kwela galimoto yakuda Isuzu zina sikha galimoto mo ndikuza londola anyamata awili ndikuza wombela mutu worse wo ...... zoti 菱 panopa tili pamalilo tikulira Koma tilibe ndalama zokhatengela Malilo Kumochale Kuti apite kumanda NDIYE timapemba akufu kwabwino. Nanga nditele mwapedza mwayi mwatengedwa kupitha kumalo kwina kwake kukhagira m'chito NDIYE kumalo kudja sakukupasa malipilo Ako mokwanira komaso magifiti ako amene amakutumizira azizako amakubelaso ndiye kuyesera kukhamba nawo akubanja kwaabwana wo palibe chinachili chose cholangula Kuma ngowopwedza nawo muliinu munga tani?Ndiwozi ndi khadja ndi masegula nadzo m'mimba komaso mowa wu wina wamwalira nawo fodja amene ndima Konda kusutayu ambiri akufa naso mmmm koma ine ndisiye kugirisa m'chito dzithu dzakupa! Ndina siyila pomwepo mukhana khala inu mukhana tani?Nanga nditele mwapedza mwayi mwatengedwa kupitha kumalo kwina kwake kukhagira m'chito NDIYE kumalo kudja sakukupasa malipilo Ako mokwanira komaso magifiti ako amene amakutumizira azizako amakubelaso ndiye kuyesera kukhamba nawo akubanja kwaabwana wo palibe chinachili chose cholangula Kuma ngowopwedza nawo muliinu munga tani?Ufulu ake sitikwawona anthu anu akamadanda ula kuti tilibe chakudja inu mumati musapepuse malawi kuli chakudja kuno . Chosecho achimwene anu m'mimba muku bwata mukha ndi njala ,chemwali ,akholo,agogo,dzidzukhuru ndi adzizanu wose mumati inu azelu . Koma bwanji iwe wekha kumaziwona ngati wazelu.Chosecho mumachita kuthandizida kuti muwoneke mmene muwonekeramo. Muziyamikha chomwe amakupangira mulungu mulungu sangandisiye ndekha mulungu ali nane. Ollo anthu oyipaa!!!! Inu opanda chisoni ndi chifundo pomarangula dza ine ndi nayamba ndatenga china chake kwanukho kuti uku gulu ranga likufuna dzopusa zakodzo ufune wina amene muzimu panga kuti aziva zakhod
Read More